Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

a N’kutheka kuti mawu amenewa akunena zimene woyang’anira malo ozungulira kachisi ku Yerusalemu ankachita. M’kati mwa usiku, iye ankayendera kachisiyo kuti aone ngati alonda achilevi, amene ankalondera malo osiyanasiyana pakachisiyo ali m’maso kapena ngati akugona. Mlonda aliyense wopezeka akugona ankamumenya ndi ndodo, ndipo zovala zake ankatha kuzitentha. Ichi chinali chilango chochititsa manyazi.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena