Mawu a M'munsi
a Buku lakuti The Jewish Encyclopedia la chaka cha 1910 linati: “Chikhulupiriro chakuti mzimu umapitiriza kukhalako thupi likafa, changokhala nzeru zaumunthu kapena malingaliro achipembedzo. Chimenechi si chiphunzitso chofunika, ndipo palibe paliponse m’Malemba Oyera pamene chimapezeka.