Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

b Baibulo silinena kuti “munga m’thupi” umene Paulo anali nawowu unali chiyani makamaka. N’kutheka kuti mwina unali vuto linalake, monga vuto la maso. N’kuthekanso kuti mawu akuti “munga m’thupi” ankatanthauza atumwi onyenga ndi anthu enanso amene ankatsutsa kuti Paulo anali mtumwi weniweni, n’kumalimbana ndi utumiki wake.​—2 Akorinto 11:6, 13-15; Agalatiya 4:15; 6:11.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena