Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

b Enosi asanabadwe, Yehova analankhula ndi Adamu. Ndipo Abele anapereka nsembe kwa Yehova yomwe Yehovayo anailandira. Komanso Mulungu analankhula ndi Kaini asanaphe mbale wake pokwiya ndi nsanje. Motero, kuyamba “kutchula dzina la Yehova” kumeneku kuyenera kuti kunali mwa njira yachilendo, osati pa kupembedza koyera.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena