Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

b Mofanana ndi zimenezi, pofotokoza za ubale watsopano wa pakati pa Mulungu ndi “ana” ake odzozedwa ndi mzimu, Paulo anagwiritsa ntchito mfundo ya zamalamulo yomwe inali yodziwika kwa anthu a mu Ufumu wa Roma omwe anawerenga kalata yake. (Aroma 8:14-17) Buku lakuti St. Paul at Rome limati: “Aroma, pachikhalidwe chawo, ankatha kutenga mwana wa wina n’kumulera kukhala wawo, ndipo umenewu ndiwo unali mchitidwe wofala m’mabanja a Aroma.”

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena