Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

c Malumbiro olemekeza Mulungu amene timagwiritsa ntchito, ngati kwanuko kulibe malamulo amene angapangitse kuti malumbirowa asinthidwe, ndi awa. Mkwati amanena kuti: “Ine [dzina la mkwati] ndikukutenga iwe [dzina la mkwatibwi] kukhala mkazi wanga wamtchatho, amene ndidzam’konda ndi kum’samalira, kunthawi yonse imene awirife tidzakhala ndi moyo padziko lapansi, momvera lamulo la Mulungu kwa amuna achikristu, loperekedwa m’Malemba Oyera, molingana ndi makonzedwe a Mulungu a ukwati.” Mkwatibwi amanena kuti: “Ine [dzina la mkwatibwi] ndikukutengani inu a [dzina la mkwati] kukhala mwamuna wanga wamtchatho, amene ndidzam’konda ndi kum’samalira ndi kum’lemekeza kwambiri, kunthawi yonse imene awirife tidzakhala ndi moyo padziko lapansi, momvera lamulo la Mulungu kwa akazi achikristu, loperekedwa m’Malemba Oyera, molingana ndi makonzedwe a Mulungu a ukwati.”

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena