Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

a Malemba amagwiritsa ntchito mawu akuti “kuwala” m’njira zosiyanasiyana zophiphiritsa. Mwachitsanzo, Baibulo limati Mulungu ndi kuwala. (Salmo 104:1, 2; 1 Yohane 1:5) Ndiponso limayerekezera kuwala ndi mfundo zonena za Mulungu zopezeka m’Mawu ake. (Yesaya 2:3-5; 2 Akorinto 4:6) Pa utumiki wake padziko lapansi, Yesu anali kuwala. (Yohane 8:12; 9:5; 12:35) Ndipo otsatira a Yesu analamulidwa kuti aonetse kuwala kwawo.​—Mateyo 5:14, 16.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena