Mawu a M'munsi
a Mawu a Chigiriki omwe anamasuliridwa kuti “anagwetsa misozi” nthawi zambiri amatanthauza “kusisima.” Koma mawu amene anawagwiritsira ntchito pofotokoza kulira kwa Mariya ndi anthu ena aja angatanthauze “kulira mofuula kapena kubuma.”