Mawu a M'munsi
b M’mbuyomu magazini ino inafotokoza kuti mbewu ikuimira makhalidwe a munthu ofunikira kukula mpaka kukhwima, ndipo kakulidwe ka makhalidwewo kamakhudzidwa ndi zinthu monga malo ndi anthu okhala nawo. Komabe, onani kuti m’fanizo la Yesu mbewu sikusintha kukhala yoipa kapena yovunda. Ikungokula mpaka kukhwima.—Onani Nsanja ya Olonda ya Chingelezi ya June 15, 1980, masamba 17-19.