Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

c Panthawi imene Yesu ankayamba utumiki wake, Yosefe ayenera kuti anali atamwaliradi, chifukwa mabuku a uthenga wabwino amangotchula za amayi, ang’ono, ndi alongo ake a Yesu okha basi. Mwachitsanzo, paukwati wa ku Kana, Mariya analipo ndipo ankagwira nawo ntchito zina, koma palibe umboni uliwonse wosonyeza kuti Yosefe analipo. (Yohane 2:1-11 ) M’nkhani ina, anthu a m’tawuni ya kwawo kwa Khristu sanatchule Yesu kuti ndi mwana wa Yosefe, koma anamutchula kuti “mwana wa Mariya.”​—Maliko 6:3.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena