Mawu a M'munsi
a Mawu a Chiheberi amene anawamasulira kuti “Beteli” amatanthauza “Nyumba ya Mulungu.” Pa mizinda yotchuka kwambiri yotchulidwa m’Baibulo, mzinda wa Beteli umaposedwa ndi mzinda wa Yerusalemu wokha basi.
a Mawu a Chiheberi amene anawamasulira kuti “Beteli” amatanthauza “Nyumba ya Mulungu.” Pa mizinda yotchuka kwambiri yotchulidwa m’Baibulo, mzinda wa Beteli umaposedwa ndi mzinda wa Yerusalemu wokha basi.