Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

a Mbali zina zofunika kukambirana m’bukuli, zili ndi mfundo zimene zingathandize anthu a misinkhu yonse. Mwachitsanzo, bokosi lakuti, “Yesetsani Kuti Musapse Mtima Kwambiri,” patsamba 221 lingathandize inuyo limodzi ndi ana anu. N’chimodzimodzinso ndi timabokosi takuti, “Mmene Mungakonzekerere,” (patsamba 132 ndi 133) “Bajeti ya Mwezi Uliwonse,” (patsamba 163) ndiponso kakuti, “Zolinga Zanga” (patsamba 314).

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena