Mawu a M'munsi
a Ena amaganiza kuti mawu a Yesu olembedwa pa Yohane 20:22, 23 amasonyeza kuti pali anthu ena amene ali ndi udindo wokhululukira machimo. Kuti mumve zambiri pa nkhani imeneyi, werengani Nsanja ya Olonda, ya April 15, 1996, tsamba 28 ndi 29.