Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

a Koma mwina tsiku limeneli silingafanane ndi limene Ayuda amachita Pasika masiku ano. N’chifukwa chiyani zili choncho? Ayuda ambiri masiku ano amachita Pasika pa Nisani 15 chifukwa amakhulupirira kuti lamulo la pa Ekisodo 12:6 linkanena kuti azichita Pasika pa Nisani 15. (Werengani Nsanja ya Olonda ya February 15, 1990, tsamba 14.) Kuti mudziwe zambiri zokhudza mmene mungawerengere masiku kuti mupeze tsiku limeneli, werengani Nsanja ya Olonda yachingerezi ya June 15, 1977, tsamba 383 mpaka 384.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena