Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

b Lemba la Levitiko 19:18 limanena kuti: “Usabwezere choipa kapena kusungira chakukhosi anthu amtundu wako. Uzikonda mnzako mmene umadzikondera wekha.” Atsogoleri a chipembedzo chachiyuda ankanena kuti mawu akuti “anthu amtundu wako” ndiponso “mnzako” amanena za Ayuda okha. Chilamulo chinkauza Aisiraeli kuti azikhala osiyana ndi anthu a mitundu ina. Komabe, sichinkalimbikitsa maganizo amene atsogoleri achipembedzo ankalimbikitsa m’nthawi ya atumwi. Atsogoleriwo ankati munthu aliyense wa mtundu wina anali mdani wawo ndipo sanali woyenera kumukonda.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena