Mawu a M'munsi
b Mawu a Paulo amenewa ndi ofanana ndi ulosi woyambirira wa m’Baibulo wolembedwa pa Genesis 3:15 umene umasonyeza kuti Mdyerekezi adzawonongedwa. Pofotokoza zimene zidzachitikezo, Paulo anagwiritsa ntchito mawu achigiriki amene amatanthauza “kuswa chinthu n’kukhala zidutswazidutswa.”—Vine’s Complete Expository Dictionary of Old and New Testament Words.