Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

a Zimbalangondo zoderapo za ku Siriya, zimene zinkapezeka ku Palesitina, zinkakhala zikuluzikulu zolemera pafupifupi makilogalamu 140. Zimbalangondo zimenezi zinkatha kupha munthu kapena nyama ndi mapazi awo akuluakulu. M’dera limeneli munkapezekanso mikango yambiri. Lemba la Yesaya 31:4 limanena kuti ngakhale “abusa ambirimbiri” sakanatha kuthamangitsa “mkango wamphamvu” kuti usiye nyama imene wagwira.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena