Mawu a M'munsi
a Mabuku a mbiri yakale amatchula zaka ziwiri zonsezi koma kuti zikhale zophweka, mu nkhanizi tigwiritsa ntchito chaka cha 587 B.C.E. Zilembo zakuti B.C.E. zimatanthauza Zaka Zathu Zino Zisanafike (m’Chingelezi, “Before the Common Era”).