Mawu a M'munsi
c Ufumu Wachiwiri wa Babulo unayamba ndi ulamuliro wa Nabopolassar, yemwe anali bambo ake a Nebukadinezara ndipo unatha ndi ulamuliro wa Nabonidus. Nthawi imeneyi ndi yofunika kwambiri kwa akatswiri amaphunziro chifukwa mbali yaikulu ya zaka 70 zija inali mkati mwa nthawi imeneyi.