Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

e Mapale a nkhani zachuma amene alipo amanena za zaka zonse za ulamuliro wa mafumu amene amati analamulira mu Ufumu Wachiwiri wa Babulo. Tikaphatikiza zaka zonse zimene mafumuwa analamulira, n’kuwerengetsera chobwerera m’mbuyo kuyambira pa Nabonidus, mfumu yomaliza mu ufumuwu, zimasonyeza kuti Yerusalemu anawonongedwa m’chaka cha 587 B.C.E. Komabe, kawerengedwe kameneka kangakhale kolondola pokhapokha ngati mfumu iliyonse yatsopano inkayamba kulamulira nthawi yomweyo mfumu ina ikangosiya kulamulira.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena