Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

b N’zochititsa chidwi kuti Zamora anagwiritsa ntchito dzina la Mulungu, osati dzina laudindo chabe, m’kalata yake yodandaula yopita kwa papa ku Rome. M’kalata ya Zamora yomwe inamasuliridwa m’Chisipanishi, dzina la Mulungu limeneli linalembedwa kuti “Yahweh.” Sizikudziwika kuti dzinali linalembedwa bwanji m’kalata yake yoyambirira ya m’Chilatini imene inatumizidwa kwa papa. Koma ponena za mabuku amene Zamora anamasulira ndiponso mmene anagwiritsira ntchito dzina la Mulungu, onani bokosi lakuti “Kumasulira Dzina la Mulungu,” patsamba 19.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena