Mawu a M'munsi
b M’mabuku achigiriki munalibe mawu amenewa. Komabe anthu anafukula zolemba zakale zokhala ndi mawu amenewa pamalo amene panali mzinda wa Tesalonika ndipo zina mwa zolembazi zinalembedwa m’nthawi ya atumwi. Zinthu zimenezi zimatsimikizira kuti nkhani za m’buku la Machitidwe ndi zolondola.