Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

b Ngakhale kuti mayiko a Britain ndi United States analipo m’zaka za m’ma 1700, Yohane ankafotokoza mmene ulamuliro wamphamvu padziko lonse wa mayikowa udzakhalire kumayambiriro kwa tsiku la Ambuye. Masomphenya a m’buku la Chivumbulutso amakwaniritsidwa “m’tsiku la Ambuye.” (Chiv. 1:10) Mutu wa 7 unaonekera kwenikweni pa nthawi ya nkhondo yoyamba ya padziko lonse pamene mayiko a Britain ndi United States anayamba kugwirizana ngati ulamuliro wamphamvu umodzi padziko lonse.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena