Mawu a M'munsi
c Danieli anaona kuti mfumuyi idzasakaza zinthu zambiri pa nthawi ya nkhondoyi. Iye analemba kuti: “Idzawononga zinthu zambiri.” (Dan. 8:24) Mwachitsanzo, dziko la United States linasakaza zambiri pamene linaponya mabomba awiri anyukiliya m’dziko limene linkadana ndi ulamuliro wa Britain ndi America.