Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

c Lamulo limeneli linali lachilendo kwambiri kwa Rute chifukwa kwawo kunalibe lamulo lotere. Kale ku Middle East akazi amasiye ankazunzika ndipo buku lina linati: “Mwamuna akamwalira, nthawi zambiri mkazi ankadalira ana ake aamuna. Ngati alibe ana, ankadzigulitsa ku ukapolo, apo ayi ankafunika kusankha kuyamba uhule kapena kungofa.”

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena