Mawu a M'munsi
c Lamulo limeneli linali lachilendo kwambiri kwa Rute chifukwa kwawo kunalibe lamulo lotere. Kale ku Middle East akazi amasiye ankazunzika ndipo buku lina linati: “Mwamuna akamwalira, nthawi zambiri mkazi ankadalira ana ake aamuna. Ngati alibe ana, ankadzigulitsa ku ukapolo, apo ayi ankafunika kusankha kuyamba uhule kapena kungofa.”