Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

c Lemba la Danieli 2:44 limanena za “kuthetsa maufumu ena onsewo.” Apa akunena za maufumu omwe akuimiridwa ndi mbali zosiyanasiyana za chifanizirochi. Koma ulosi wina m’Baibulo umanena kuti “mafumu a dziko lonse lapansi” adzasonkhanitsidwa kuti alimbane ndi Yehova pa “tsiku lalikulu la Mulungu Wamphamvuyonse.” (Chiv. 16:14; 19:19-21) Choncho maufumu a m’chifanizirocho komanso maufumu onse a padziko lapansi adzawonongedwa pa Aramagedo.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena