Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

b Monga Naomi ananenera, Yehova amasonyeza kukoma mtima kwa anthu, ngakhalenso amene anamwalira. Mwamuna wa Naomi komanso ana ake awiri anali atamwalira. Ndipo mmodzi mwa ana a Naomi amene anamwalirawo, anali mwamuna wake wa Rute. N’zosakayikitsa kuti amuna atatu onsewa ankakonda kwambiri Naomi ndi Rute. Choncho kukomera mtima Naomi ndi Rute tingati kunalinso kukomera mtima amunawo chifukwa iwo akanakonda kuti azimayiwa azisamalidwa.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena