Mawu a M'munsi
e Rute ndi mmodzi mwa akazi anayi amene Baibulo limatchula pa mzere wa makolo a Yesu. Wina ndi Rahabi, yemwe anali mayi ake a Boazi. (Mateyu 1:3, 5, 6) Mofanana ndi Rute, nayenso Rahabi sanali Mwisiraeli.
e Rute ndi mmodzi mwa akazi anayi amene Baibulo limatchula pa mzere wa makolo a Yesu. Wina ndi Rahabi, yemwe anali mayi ake a Boazi. (Mateyu 1:3, 5, 6) Mofanana ndi Rute, nayenso Rahabi sanali Mwisiraeli.