Mawu a M'munsi
a Onani nkhani yakuti, “Kodi N’chifukwa Chiyani Ndiyenera Kudziwana ndi Agogo Anga?” mu Galamukani! ya May 8, 2001 ndi yakuti, “Kodi Nditani Kuti Ubale Wanga ndi Agogo Ulimbe?” mu Galamukani! ya June 8, 2001. Magaziniwa ndi ofalitsidwa ndi Mboni za Yehova.