Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

a Nanga bwanji ngati kamwanako m’mimba mwa mayiyo kakuoneka kuti sikadzabadwa kabwinobwino, kapenanso ngati zikuoneka kuti adzabereka ana angapo? Zikatero, ena amasankha kuchotsa mimbayo. Amayi amene amatsatira njira yochotsa mazira m’mimba n’kukawaphatikiza ndi umuna, nthawi zambiri amabereka ana awiri, atatu kapena kuposerapo. Zimenezi zimabweretsa mavuto monga kubereka ana masiku asanakwane ndiponso kutaya magazi ambiri pobereka. Chotero mayi amene akuoneka kuti adzabereka ana ambiri amamulimbikitsa kuti asankhe ana oti abereke ndipo enawo awaphe. Kuchita zimenezi n’kuchotsa mimba kwadala ndipo n’chimodzimodzi ndi kupha munthu.—Eks. 21:22, 23; Sal. 139:16.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena