Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

a Palembali mawu akuti “pamene dziko linakhazikika” amanena za kuberekana kwa anthu, choncho lembali likunena za ana a anthu oyambirira. Nanga n’chifukwa chiyani Yesu ananena za Abele, kuti anakhalapo “pamene dziko linakhazikika” pomwe woyamba kubadwa anali Kaini? N’chifukwa choti zochita za Kaini zinasonyeza kuti anali wopandukira Yehova Mulungu. Mofanana ndi makolo ake, zikuoneka kuti Kaini sali m’gulu la anthu odzaukitsidwa komanso kuwomboledwa ku uchimo ndi imfa.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena