Mawu a M'munsi
a Abale ndi alongowo anafunsidwanso kuti, “Kodi mumafuna kuti mkulu akhale ndi khalidwe liti?” Ambiri mwa iwo ananena kuti amafuna kuti akhale wochezeka. Tidzakambirana khalidwe lofunika limeneli m’magazini yam’tsogolo.
a Abale ndi alongowo anafunsidwanso kuti, “Kodi mumafuna kuti mkulu akhale ndi khalidwe liti?” Ambiri mwa iwo ananena kuti amafuna kuti akhale wochezeka. Tidzakambirana khalidwe lofunika limeneli m’magazini yam’tsogolo.