Mawu a M'munsi
b Mawu akuti “atumwi 12 aja” akunena za “atumwi okhulupirika” ngakhale kuti pa nthawi ina Yudasi Isikariyoti atafa, atumwi analipo 11 okha. Pa nthawi inanso pamene Yesu ankaonekera kwa atumwi, panali atumwi 10 okha chifukwa Tomasi panalibe. Komabe atumwi 10 amenewa anaimira atumwi 12.—Yohane 20:24.