Mawu a M'munsi
b Ndime 8: Chinthu chimodzi chimene chatchulidwa m’mavesi amenewa ndi ‘kusonkhanitsa osankhidwa.’ (Mat. 24:31) Choncho zikuoneka kuti odzozedwa onse amene adzakhale padzikoli mbali yoyamba ya chisautso chachikulu ikadzatha, adzatengedwa kupita kumwamba nkhondo ya Aramagedo isanayambe. Izi zikusintha zimene zinafotokozedwa m’nkhani ya “Mafunso Ochokera kwa Owerenga” mu Nsanja ya Olonda ya August 15, 1990, tsamba 30.