Mawu a M'munsi
b Ndime 3: Popeza atumwi a Yesu anali atamwalira ndipo odzozedwa amene anatsala padzikoli ankaimiridwa ndi tirigu, akapolo amenewa akuimira angelo. Komanso m’fanizo lomweli Yesu ananena kuti osonkhanitsa namsongole ndi angelo.—Mat. 13:39.