Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

e Ndime 14: Izi zikusintha zimene tinkakhulupirira pa lemba la Mateyu 13:42. Poyamba, tinkafotokoza m’mabuku athu kuti Akhristu onyenga akhala ‘akulira ndi kukukuta mano’ kwa zaka zambiri chifukwa chakuti “ana a ufumu” akuwaulula kuti ndi “ana a woipayo.” (Mat. 13:38) Komabe Baibulo limasonyeza kuti nthawi imene anthu adzakukute mano m’pamene adzawonongedwa.—Sal. 112:10.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena