Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

b Akatswiri ofukula zinthu zakale apeza nsanja zazitali zokhala ndi masitepe ku Sinara. Baibulo limanena kuti anthu amene ankamanga nsanja ya Babele ankamangira njerwa, osati miyala, ndipo ankagwiritsa ntchito phula mmalo mwa matope. (Genesis 11:3, 4) Buku la The New Encyclopædia Britannica linanena kuti ku Mesopotamiya miyala inali “yosowa kwambiri, mwinanso sinkapezeka n’komwe,” pamene phula linkapezeka lambiri.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena