Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

b Tsiku la Nisani 15 linali tsiku loyamba la Chikondwerero cha Mikate Yopanda Chofufumitsa ndipo nthawi zonse linkakhala tsiku la sabata. Koma m’chaka cha 33 C.E. tsikuli linali pa Loweruka, lomwe mlungu uliwonse linkakhala la sabata. Choncho popeza kuti tsiku la Nisani 15 mu 33 C.E. linali la sabata pa zifukwa ziwiri zimenezi, ankanena kuti linali Sabata “lalikulu.”—Werengani Yohane 19:31, 42.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena