Mawu a M'munsi
a Katswiri wina wa ku Germany ananena kuti: “Popeza . . . Yesu analipo ndipo thupi lake lonse linali labwinobwino komanso magazi ake anali asanakhetsedwe, palibe aliyense mwa atumwiwo amene akanaganiza . . . zoti akudya thupi lenileni kapena kumwa magazi enieni a Ambuye. Choncho Yesu anagwiritsa ntchito mawu osavuta pofotokoza zimenezi ndipo sakanafuna kuti ophunzira ake amve zina.”