Mawu a M'munsi
a Atangolemba kalata ya 1 Akorinto, Paulo anauyamba ulendo wopita ku Makedoniya kudzera ku Torowa. Ali ku Makedoniyako analemba kalata ya 2 Akorinto. (2 Akor. 2:12; 7:5) Ndiyeno atachoka kumeneko anafika ku Korinto.
a Atangolemba kalata ya 1 Akorinto, Paulo anauyamba ulendo wopita ku Makedoniya kudzera ku Torowa. Ali ku Makedoniyako analemba kalata ya 2 Akorinto. (2 Akor. 2:12; 7:5) Ndiyeno atachoka kumeneko anafika ku Korinto.