Mawu a M'munsi
a Nkhani yomaliza ya m’Baibulo yomwe imatchula Yosefe, ndi yonena za zimene zinachitika Yesu ali ndi zaka 12. Kuchokera pa nthawiyi, Baibulo limangotchula za amayi a Yesu ndi azibale ake basi, koma osati Yosefe. Komanso pa nthawi ina Yesu ankatchedwa “mwana wa Mariya,” popanda kutchula Yosefe.—Maliko 6:3.