Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

a M’nkhaniyi mawu akuti kusuta, akunena za kulowetsa utsi wa fodya m’mapapo kudzera mu ndudu, fodya wopichira, kaliwo komanso kugwiritsa ntchito chipangizo chimene chimachititsa kuti utsi wa fodya uzidutsa m’madzi, usanalowe m’thupi. Komabe mfundo zomwe zili m’nkhaniyi zikukhudzanso fodya wotafuna, wofwenkha ndi wina wotero.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena