Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

a Akatswiri ena amati azichimwene ake a Yosefe anaona kuti bambo awo anapatsa Yosefe mkanjo chifukwa ankafuna kuti Yosefeyo adzatenge madalitso amene ankaperekedwa kwa mwana woyamba kubadwa. Ankadziwanso kuti Yosefe anali mwana woyamba wa Rakele, mkazi amene Yakobo ankamukonda kwambiri. Komanso Rubeni, mwana woyamba wa Yakobo, anali atagona ndi Biliha, mkazi wamng’ono wa bambo ake. Uku kunali kunyoza bambo akewo komanso kupeputsa udindo wake monga mwana woyamba.—Genesis 35:22; 49:3, 4.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena