Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

a Ngakhale kuti dzina la Mulungu linkapezeka kambirimbiri m’Malemba Achiheberi, omwe ambiri amati Chipangano Chakale, n’zomvetsa chisoni kuti anthu ambiri omasulira Mabaibulo sanaike dzinali m’Mabaibulo amene anamasulira. Pamene panali dzinali anaikapo mayina audindo monga akuti, “Ambuye” kapena “Mulungu.” Kuti mudziwe zambiri pa nkhaniyi, werengani tsamba 195 mpaka 197 m’buku lakuti, Kodi Baibulo Limaphunzitsa Chiyani Kwenikweni? lofalitsidwa ndi Mboni za Yehova.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena