Mawu a M'munsi
a Ngakhale kuti dzina la Mulungu linkapezeka kambirimbiri m’Malemba Achiheberi, omwe ambiri amati Chipangano Chakale, n’zomvetsa chisoni kuti anthu ambiri omasulira Mabaibulo sanaike dzinali m’Mabaibulo amene anamasulira. Pamene panali dzinali anaikapo mayina audindo monga akuti, “Ambuye” kapena “Mulungu.” Kuti mudziwe zambiri pa nkhaniyi, werengani tsamba 195 mpaka 197 m’buku lakuti, Kodi Baibulo Limaphunzitsa Chiyani Kwenikweni? lofalitsidwa ndi Mboni za Yehova.