Mawu a M'munsi
a Nsanja ya Olonda ya July 15, 2013, tsamba 21 mpaka 22, ndime 8 mpaka 10, inafotokoza mfundo zotithandiza kudziwa kapolo wokhulupirika ndi wanzeru. Nkhani yapitayi yafotokoza tanthauzo la fanizo la anamwali 10. Fanizo la nkhosa ndi mbuzi linafotokozedwa mu Nsanja ya Olonda ya October 15, 1995, tsamba 23 mpaka 28 ndiponso lifotokozedwa m’nkhani yotsatira.