Mawu a M'munsi
d Atumwi atamwalira, Satana anayambitsa mpatuko. Mpatukowo unasokoneza mpingo wachikhristu kwa zaka zambiri. Pa nthawiyi, palibe anthu amene ankapitiriza ntchito imene Yesu anaisiya. Koma izi zinadzasintha ‘m’nthawi yokolola’ kapena kuti m’masiku otsiriza. (Mat. 13:24-30, 36-43) Onani Nsanja ya Olonda ya July 15, 2013, tsamba 9 mpaka 12.