Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

a Buku lina linanena kuti “pogwiritsa ntchito njirayi, akatswiri amatha kudziwa nthawi imene zinthu zinalembedwa. Amayerekezera kalembedwe ka chinthu chimene akufuna kufufuzacho, ndi kalembedwe ka zinthu zina zakale.” (Manuscripts of the Greek Bible) Pa nthawi inayake anthu amakhala ndi kalembedwe kofanana, koma pakapita nthawi zimasintha ndipo amayamba kalembedwe kena. Choncho akatswiriwa amatha kuzindikira nthawi yomwe chinthu chinalembedwa poona kalembedwe kake.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena