Mawu a M'munsi
a M’chaka cha 2012, bungwe lina linachita kafukufuku ku United States. Bungweli linapeza kuti anthu 11 pa anthu 100 alionse omwe sakhulupirira kuti kuli Mulungu kapena omwe amakayikira zoti kuli Mulungu, amapemphera kamodzi pa mwezi.