Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

a Zikuoneka kuti ambiri mwa anthuwa anadzakhala Akhristu. Tikutero chifukwa chakuti m’kalata imene Paulo analembera Akhristu a ku Korinto, ananena kuti anthu oposa 500 aja tsopano anali “abale.” Iye ananenanso kuti: “Ambiri a iwo akali ndi moyo mpaka lero, koma ena anagona mu imfa.” Choncho zikuoneka kuti Paulo ankadziwana ndi ena mwa Akhristu amene analipo pamene Yesu ankapereka lamulo loti ophunzira ake azilalikira.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena