Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

b Dzina la Baibuloli limatanthauza 70 ndipo ena amaganiza kuti linamasuliridwa ndi anthu 72. Zikuoneka kuti Baibuloli linayamba kumasuliridwa ku Iguputo pafupifupi zaka 300 Yesu asanabadwe ndipo n’kutheka kuti linamalizidwa patapita zaka 150. Baibulo limeneli ndi lofunikabe masiku ano chifukwa limathandiza akatswiri a Baibulo kumvetsa tanthauzo la mawu kapena mavesi ena a m’Malemba Achiheberi.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena